Msonkhano wacigawo wapadela ku Vienna, m’dziko la Austria

UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO July 2018

Makambilano Acitsanzo

Makambilano otsatizana-tsatizana a mmene mfundo za m’Baibo zimathandizila mabanja kukhala acimwemwe.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Tizipimila Ena Mowolowa Manja

Munthu wowolowa manja amathandiza ena mokondwela na kuwalimbikitsa.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Khala Wotsatila Wanga—Motani?

Kodi tifunika kusumika maganizo athu pa ciani ngati tayamba kuganizila zinthu zakale zimene zingaticenjeneke?

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Fanizo la Msamariya Wacifundo

Otsatila a Yesu afunika kuyesetsa kukonda anthu, ngakhale amene aoneka kuti ni osiyana nawo kwambili.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

N’cifukwa Ciani Kusatengako Mbali Mundale N’kofunika? (Mika 4:2)

Potengela Mulungu wathu wopanda tsankho, tifunika kucitila anthu onse zabwino.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

“Ndinu Ofunika Kwambili Kuposa Mpheta Zambili”

Tingatengele bwanji citsanzo ca Yehova pankhani yodela nkhawa anthu amene akuzunzidwa?

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

Fanizo la Mwana Woloŵelela

Kodi fanizo ili litiphunzitsa ciani pa nkhani ya kukhala wozindikila, kudzicepetsa, na kudalila Yehova Mulungu?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Mwana Woloŵelela

Kodi mu vidiyo imeneyi titengamo maphunzilo ofunika ati?