July 23-29
LUKA 12-13
Nyimbo 4 na Pemphelo
Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
“Ndinu Ofunika Kwambili Kuposa Mpheta Zambili”: (10 min.)
Luka 12:6—Ngakhale mbalame zing’ono-zing’ono Mulungu saziiŵala (“mpheta” nwtsty mfundo younikila)
Luka 12:7—Yehova amatidziŵa bwino kwambili. Uwu ni umboni wakuti amatikonda ngako (“ngakhale tsitsi lonse la m’mutu mwanu analiŵelenga” nwtsty mfundo younikila)
Luka 12:7—Yehova amaona aliyense wa ise kukhala wofunika (cl peji 241 mapa. 4-5)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Luka 13:24—Kodi zimene Yesu anakamba pa lembali zitanthauza ciani? (“Yesetsani mwamphamvu” nwtsty mfundo younikila)
Luka 13:33—N’cifukwa ciani Yesu anakamba mau amenewa? (“n’kosayenela” nwtsty mfundo younikila)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Luka 12:22-40
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Kubwelelako Kaciŵili: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno itanilani mwininyumba ku misonkhano.
Kubwelelako Kacitatu: (3 min. olo kucepelapo) Sankhani mwekha lemba, ndipo gaŵilani cofalitsa cophunzitsila Baibo.
Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) lv mape. 184-185 mapa. 4-5
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Sayenda Koma Sanaiŵalidwe: (15 min.) Tambitsani vidiyoyi. Pambuyo pake, kambilanani mafunso aya:
Kodi ofalitsa atatuwa anakumana na mavuto anji?
Kodi Yehova anawaonetsa bwanji kuti sanawaiŵale?
Kodi ofalitsawo anapitiliza bwanji kutumikila Yehova ngakhale kuti anakumana na mavuto? Nanga kucita zimenezi kunawalimbikitsa bwanji ofalitsa ena?
Kodi okalamba kapena odwala amene ali mu mpingo wanu mungawaonetse bwanji cikondi?
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy Mutu 30
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 5 na Pemphelo