CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Anadzimana Zinazake Cifukwa Comvela Yehova
Mabanja ena anapemphedwa kusiya nyumba na minda yawo kuti akakhale mumzinda wa Yerusalemu (Neh. 11:1; w98 10/15 22 ¶13)
Amene anadzipeleka kucita zimenezi anadalitsidwa (Neh. 11:2; w86 2/15 26)
Madalitso a Yehova nthawi zonse amakhala oculuka kuposa zilizonse zimene tingadzimane (Malaki 3:10; w16.04 7 ¶15)
DZIFUNSENI KUTI, ‘Ni madalitso otani amene napeza cifukwa codzimana kuti nitumikile Yehova?’