Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

July 31–August 6

NEHEMIYA 3-4

July 31–August 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Kodi Mumaona Kuti Nchito Yamanja si Yokuyenelelani?”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • Neh. 4:17, 18—Kodi munthu angagwile bwanji nchito na dzanja limodzi? (w06 2/1 9 ¶1)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo iti yokupindulilani imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Neh. 3:15-24 (th phunzilo 2)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. Mukayamba, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 3)

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Kambilanani mfundo za pa cikuto ca kumbuyo ca bulosha yakuti Kondwelani na Moyo Kwamuyaya!, na kum’pempha kuti muziphunzila naye Baibo. (th phunzilo 12)

  • Nkhani: (Mph. 5) km 11/12 1—Mutu: Sangalalani Cifukwa Cakuti Mwagwila Nchito Mwakhyama. (th phunzilo 10)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 91

  • Kuseŵenza na Mboni za Yehova: (Mph. 8) Kukambilana. Onetsani vidiyoyi. Kenako funsani omvela funso ili: Malinga na vidiyo imeneyi, kodi khalidwe lathu kunchito lingacitile bwanji umboni?

  • Zofunikila za Mpingo: (Mph. 7)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff phunzilo 52

  • Mawu Othela (Mph. 3)

  • Nyimbo 29 na Pemphelo