August 12-18
MASALIMO 73-74
Nyimbo 36 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)
1. Kodi Tingacite Ciyani Ngati Timacitila Nsanje Anthu Omwe Salambila Mulungu?
(Mph.10)
Tingayambe kucitila nsanje anthu omwe salambila Mulungu (Sal. 73:3-5; w20.12 19 ¶14)
Tingayambe kuona zinthu moyenela ngati tilambila pamodzi na abale anzathu m’malo modzipatula (Sal. 73:17; Miy. 18:1; w20.12 19 ¶15-16)
Anthu amene salambila Mulungu ali “pamalo otelela,” koma anthu amene amalambila Mulungu amalandila “ulemelelo” (Sal. 73:18, 19, 24; w14 4/1 8 ¶5; w13-CN 2/15 25-26 ¶3-5)
2. Kufufuza Cuma Cauzimu
(Mph. 10)
Sal. 74:13, 14—Kodi “Leviyatani” ayenela kuti aimila ciyani? (it-2-E 240)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?
3. Kuŵelenga Baibo
(Mph. 4) Sal. 74:1-23 (th phunzilo 10)
4. Kuyambitsa Makambilano
(Mph. 3) ULALIKI WAMWAYI. Pezani mpata wouzako mnzanu zimene munaphunzila pa msonkhano waposacedwa. (lmd phunzilo 2 mfundo 4)
5. Kubwelelako
(Mph. 4) ULALIKI WAPOYELA. Mupempheni kuti muziphunzila naye Baibo na kumuonetsa mmene phunzilo la Baibo limacitikila. (lmd phunzilo 8 mfundo 3)
6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupilila
(Mph. 5) Nkhani. ijwbq 89—Mutu: Kodi Zipembedzo Zonse N’zabwino? (th phunzilo 14)
Nyimbo 72
7. Zofunikila za Mpingo
(Mph. 15)
8. Phunzilo la Baibo la Mpingo
(Mph. 30) bt mutu 14 ¶1-6, bokosi pa tsa. 112