Makambilano Acitsanzo
●○○ULENDO WOYAMBA
Funso: Kodi tili m’masiku otsiliza?
Lemba: 2 Tim. 3:1-5
Ulalo: N’ciani cidzacitika pambuyo pa masiku otsiliza?
○●○ULENDO WOBWELELAKO WOYAMBA
Funso: N’ciani cidzacitika pambuyo pa masiku otsiliza?
Lemba: Chiv. 21:3, 4
Ulalo: Tingacite ciani kuti tikalandile madalitso amene Mulungu walonjeza kutsogolo?
○○●ULENDO WOBWELELAKO WACIŴILI
Funso: Tingacite ciani kuti tikalandile madalitso amene Mulungu walonjeza kutsogolo?
Lemba: Yoh. 3:16
Ulalo: Kodi kukhala na cikhulupililo kumatanthauza ciani?