UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO March 2016
Maulaliki Acitsanzo
Maulaliki acitsanzo ogaŵila Nsanja ya Mlonda ndi kapepala koitanila anthu ku Cikumbutso ka 2016. Seŵenzetsani maulaliki acitsanzo amenewa kuti mukonze ulaliki wanu.
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Esitere Anaimila Yehova ndi Anthu Ake
Molimba mtima iye anaika moyo wake pangozi, ndipo anathandiza Moredekai kulemba lamulo lakuti Ayuda asaphedwe. (Esitere 6-
KUONJEZELA LUSO LANU MU ULALIKI
Kunola Luso Lathu mu Ulaliki —Konzani Ulaliki Wanu Wogaŵila Magazini
Gwilitsilani nchito maulaliki acitsanzo kuti mukonze ulaliki wanu wogaŵila Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani!
UMOYO WATHU WACIKRISTU
Landilani Alendo
Kodi tingathandize bwanji alendo ndi ozilala kudzimva kuti ndi olandilidwa pa Cikumbutso?
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Yobu Anakhalabe Wokhulupilika Pamene Anali Kuyesedwa
Iye anaonetsa kuti Yehova ndi wofunika kwambili paumoyo wake. (Yobu 1-
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Munthu Wokhulupilika Yobu Afotokoza Mavuto Ake
Mavuto aakulu amene Yobu anakumana nao anakhudza mmene iye anali kuonela zinthu, koma anapitiliza kukonda Yehova Mulungu. (Yobu 6-
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
Yobu Anali ndi Cikhulupililo Cakuti Akufa Adzauka
Anali kudziŵa kuti Mulungu adzamuukitsa, mofanana ndi kuphukilanso kwa citsa couma ca mtengo. (Job 11-
UMOYO WATHU WACIKRISTU
Ciukililo Cidzatheka Kupitila mu Nsembe ya Dipo
Mphatso ya Yehova ya dipo idzacititsa kuti ciukililo ca mtsogolo cikakhale cotheka. M’malo moika malilo, tizikalandila anthu amene adzaukitsidwa.