Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

March 20-26

YEREMIYA 8-11

March 20-26
  • Nyimbo 117 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Anthu Angapambane Kokha Ngati Atsogozedwa na Yehova”: (10 min.)

    • Yer. 10:2-5, 14, 15—Milungu ya amitundu ni milungu yonama (it-1 555)

    • Yer. 10:6, 7, 10-13—Mosiyana na milungu ya amitundu, Yehova yekha ndiye Mulungu woona (w04 10/1 peji 11 pala. 10)

    • Yer. 10:21-23—Anthu sangapambane popanda citsogozo ca Yehova (w15 9/1 peji 15 pala. 1)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yer. 9:24—Kodi kudzitama ndi kunyada koyenela n’kotani? (w13 1/15 peji 20 pala. 16)

    • Yer. 11:10—N’cifukwa ciani Yeremiya popeleka uthenga wa ciweluzo anaphatikizapo ufumu wa kumpoto wa mafuko 10 ngakhale kuti Samariya anali atawonongedwa kale mu 740 B.C.E.? (w07 3/15 peji 9 pala. 2)

    • Kodi ine pacanga, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwaniphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino zimene ine pacanga ningaseŵenzetse mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Yer. 11: 6-16

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) Ciitano ca ku Cikumbutso na nkhani ya pacikuto ca wp17.2—Yalani maziko a ulendo wobwelelako.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) Ciitano ca ku Cikumbutso na nkhani ya pacikuto ca wp17.2—Yalani maziko a ulendo wotsatila.

  • Phunzilo la Baibo: (6 mineti kapena kucepelapo) ld mapeji 4-5 (Mwininkhani angasankhe mapikica amene angakambilane.)—Itanilani munthuyo ku Cikumbutso.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU