March 5-11
MATEYU 20-21
Nyimbo 76 na Pemphelo
Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
“Aliyense Wofuna Kukhala Wamkulu Pakati Panu Ayenela Kukhala Mtumiki Wanu”: (10 min.)
Mat. 20:3—Alembi na Afarisi onyada anali kukonda kuimilila pamsika kuti anthu awaone na kuwapatsa moni (“Pamsika” nwtsty zithunzi)
Mat. 20:20, 21—Atumwi aŵili anapempha malo apamwamba ndi a ulamulilo (“mkazi wa Zebedayo” “mmodzi kudzanja lanu lamanja, wina kumanzele kwanu” Mat. 20:20, 21 nwtsty mfundo zounikila)
Mat. 20:25-28—Yesu anafotokoza kuti otsatila ake afunika kukhala atumiki odzicepetsa (“mtumiki” “sanabwele kudzatumikilidwa, koma kudzatumikila” nwtsty mfundo zounikila pa Mat. 20:26, 28)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Mat. 21:9—Kodi khamu la anthu linatanthauza ciani pamene linafuula kuti: “M’pulumutseni” “Mwana wa Davide!”? (nwtsty mfundo younikila)
Mat. 21:18, 19—N’cifukwa ciani Yesu anafotetsa mtengo wa mkuyu? (jy peji 244 mapa. 4-6)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mat. 20:1-19
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
Kubwelelako Koyamba (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.
Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) lv mape. 36-37 mapa. 3-4