March 19-25
MATEYU 24
Nyimbo 126 na Pemphelo
Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
“Khalanibe Ogalamuka m’Masiku Otsiliza Ano”: (10 min.)
Mat. 24:12—Kuwonjezeka kwa kusamvela malamulo kudzacititsa cikondi ca anthu kuzilala (it-2 peji 279 pala. 6)
Mat. 24:39—Anthu ena adzakhala na nkhawa yaikulu kufuna-funa zinthu zakuthupi, ndipo zidzawacenjeneka (w99 11/15 peji 19 pala. 5)
Mat. 24:44—Ambuye adzabwela pa nthawi yosayembekezeleka (jy peji 259 pala. 4)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Mat. 24:8—Kodi zimene Yesu anakamba zitipatsa cithunzi canji? (“zoŵaŵa za pobeleka” nwtsty mfundo younikila pa Mat. 24:8)
Mat. 24:20—N’cifukwa ciani Yesu anakamba izi? (“nyengo ya cisanu,” “pa tsiku la sabata” nwtsty mfundo younikila pa Mat. 24:20)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mat. 24:1-22
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Mwininyumba akambe zimene anthu a m’gawo lanu amakamba posafuna kulalikidwa.
Kubwelelako Koyamba: (3 min. olo kucepelelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Munthu amene munakambilana naye simunamupeze, koma mwapeza m’bululu wake.
Vidiyo ya Kubwelelako Kaciŵili: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Tili ku Mapeto a Dongosolo Lino la Zinthu”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 13
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 97 na Pemphelo