Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 15-16

Yang’anani kwa Yehova Kuti Akuthandizeni Kupilila na Kukutonthozani

Yang’anani kwa Yehova Kuti Akuthandizeni Kupilila na Kukutonthozani

15:4-7

Njila imodzi imene Yehova amatitonthozela na kutithandiza kupilila, ni kupitila m’Mawu ake. Kodi zitsanzo za m’Baibo izi zingakutonthozeni motani, komanso zingakulimbikitseni bwanji?

  • Nowa

  • Yosefe

  • Davide