Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

March 25-31

1 AKORINTO 4-6

March 25-31
  • Nyimbo 123 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Cofufumitsa Cacing’ono Cimafufumitsa Mtanda Wonse”: (10 min.)

    • 1 Akor. 5:1, 2—Mpingo wa ku Korinto unali kulekelela munthu wocita zoipa wosalapa

    • 1 Akor. 5:5-8, 13—Paulo anauza mpingowo kuti ucotse “cofufumitsa” pakati pawo na kupeleka wocita zoipayo kwa Satana (it-2 230, 869-870)

    • 1 Akor. 5:9-11—Mpingo suyenela kuyanjana ndi anthu ocita zoipa amene safuna kulapa (lvs 241, mfundo za kumapeto “Kucotsa Munthu mu Mpingo”)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • 1 Akor. 4:9—Kodi atumiki a Mulungu aumunthu ni “coonetsedwa m’bwalo la maseŵela” kwa angelo motani? (w09 5/15 24 ¶16)

    • 1 Akor. 6:3—Kodi Paulo ayenela kuti anatanthauza ciani pamene analemba kuti: “Tidzaweluza angelo”? (it-2 211)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) 1 Akor. 6:1-14 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 78

  • Seŵenzetsani Mavidiyo Pophunzitsa Anthu Baibo”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani na kukambilana vidiyo yoonetsa wofalitsa akuseŵenzetsa vidiyo ya phunzilo 4 m’bulosha ya Uthenga Wabwino, pophunzitsa wophunzila Baibo.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 60

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 23 na Pemphelo