GENESIS 25-26
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU |Esau Anagulitsa Udindo Wake Monga Woyamba Kubadwa
25:27-34
Esau ‘sanayamikile zinthu zopatulika.’ (Aheb. 12:16) Zotulukapo zake, anagulitsa udindo wake monga woyamba kubadwa. Anakwatilanso akazi aŵili amitundu ina.—Gen. 26:34, 35.
DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ningaonetse bwanji kuti nimayamikila kwambili zinthu zopatulika izi?’
-
Ubale wanga na Yehova
-
Mzimu woyela
-
Kudziŵika na dzina loyela la Yehova
-
Ulaliki
-
Misonkhano yacikhristu
-
Cikwati