Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

March 30–April 5

GENESIS 29-30

March 30–April 5

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Yakobo Akwatila”: (10 min.)

    • Gen. 29:18-20—Yakobo anavomela kuseŵenzela Labani zaka 7 kuti akwatile Rakele (w03 10/15 29 ¶6)

    • Gen. 29:21-26—Labani anapusitsa Yakobo pom’patsa Leya m’malo mwa Rakele (w07 10/1 8-9; it-2 341 ¶3)

    • Gen. 29:27, 28—Ngakhale kuti Yakobo anakumana na zovuta, anayesetsa kucita zinthu moyenela

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Gen. 30:3​—N’cifukwa ciani Rakele anakamba kuti ana amene Biliha anabeleka kwa Yakobo ni ake? (it-1 50)

    • Gen. 30:14, 15—N’cifukwa ciani Rakele ayenela kuti anataya mwayi wokhala na pakati mwa kuusinthanitsa na mandereki? (w04 1/15 28 ¶7)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mbali ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 30:1-21 (th phunzilo 2)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 57

  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kulalikila Anthu Akhungu”: (10 min.) Nkhani yokambilana yokambidwa na woyang’anila utumiki. Funsani omvetsela mafunso aya: N’cifukwa ciani tifunika kuganizila zosoŵa za anthu osaona? N’kuti kumene tingapeze anthu akhungu? Kodi tingawafikile bwanji? Ni zida ziti zimene tili nazo zothandiza anthu osaona kupita patsogolo mwauzimu?

  • Zimene Gulu Likukwanilitsa: (5 min.) Tambitsani vidiyo yakuti Zimene Gulu Likukwanilitsa ya March.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 110

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 30 na Pemphelo