CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Mmene Cikhulupililo Cimatithandizila Kukhala Olimba Mtima
Azondi amene anabweletsa uthenga wofooketsa analibe cikhulupililo (Num. 13:31-33; 14:11)
Kusoŵa cikhulupililo kwa azondi 10 kunapangitsa abale awo kutaya mtima (Num. 14:1-4)
Azondi amene anakhalabe olimba mtima anali na cikhulupililo colimba (Num. 14:6-9; w06 10/1 16-17 ¶5-6)
Aisiraeli anali ataonapo kale nchito zopulumutsa za Yehova. Izi zinayenela kulimbitsa cikhulupililo cawo cakuti iye adzawathandiza kulanda dziko la Kanani.