March 14-20
1 SAMUELI 14-15
Nyimbo 89 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kumvela Kumaposa Nsembe”: (Mph. 10)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
1 Sam. 15:24—Kodi pali cenjezo lotani pa cifundo cosayenela cimene Sauli anaonetsa? (it-1 493)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) 1 Sam. 15:1-16 (th phunzilo 2)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako: (Mph. 5) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Ulendo Wobwelelako: Yesu—Mat. 20:28. Nthawi iliyonse vidiyo ikaima, inunso iimitseni na kufunsa omvetsela mafunso amene aonekela mu vidiyo.
Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Yambani na makambilano acitsanzo. Kenako gaŵilani cofalitsa ca mu Thuboksi yathu. (th phunzilo 3)
Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Yambani na makambilano acitsanzo. Pemphani kuti muziphunzila naye Baibo. Kenako, chulani na kukambilanako za mu vidiyo yakuti Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji? (koma musaitambitse) (th phunzilo 11)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Kumemeza Anthu ku Cikumbutso Kudzayamba pa Ciŵelu, pa March 19: (Mph. 10) Kukambilana. Mwacidule, kambilanani zimene zili m’kapepala koitanila anthu ku Cikumbutso. Fotokozani makonzedwe a pampingo panu okhudza nkhani yapadela na Cikumbutso, komanso a mofolela magawo. Tambitsani na kukambilana vidiyo ya ulaliki wacitsanzo.
Khala Bwenzi la Yehova—Mvela Yehova: (Mph. 5) Kukambilana. Onetsani vidiyoyi.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb phunzilo 81
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 125 na Pemphelo