March 21-27
1 SAMUELI 16-17
Nyimbo 7 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Yehova Ndiye Mwini Nkhondo”: (10 min.)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
1 Sam. 16:14, na mawu a m’munsi.—Kodi mawu akuti Sauli analandila “mzimu woipa wocokela kwa Yehova” atanthauza ciani? (it-2 871-872)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) 1 Sam. 16:1-13 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Kumemeza Anthu ku Cikumbutso: (Mph. 2) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 11)
Kumemeza Anthu ku Cikumbutso: (Mph. 3) Itanilani mnzanu wa kunchito, wa kusukulu, kapena wacibale amene munamulalikilapo kale. (th phunzilo 2)
Ulendo Wobwelelako: (Mph. 3) Citani ulendo wobwelelako kwa munthu amene analandila kapepala koitanila anthu ku Cikumbutso, amenenso anaonetsa cidwi. (th phunzilo 4)
Ulendo Wobwelelako: (Mph. 3) Citani ulendo wobwelelako kwa munthu amene analandila kapepala koitanila anthu ku Cikumbutso, amenenso anaonetsa cidwi. M’fotokozeleni za webusaiti yathu munthuyo. (th phunzilo 20)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Njila Zitatu Zoonetsela Kuti Timadalila Yehova”: (Mph. 15) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Palibe Cifukwa Coopela Cizunzo.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb phunzilo 82
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 47 na Pemphelo