March 25-31
SALIMO 22
Nyimbo 19 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)
1. Baibo Inakambilatu Zodzacitika pa Imfa ya Yesu
(Mph. 10)
Yesu adzaoneka ngati Mulungu wamusiya (Sal. 22:1; w11 8/15 15 ¶16)
Yesu adzanyozedwa (Sal. 22:7, 8; w11 8/15 15 ¶13)
Anthu adzacita maele pa zovala za Yesu (Sal. 22:18; w11 8/15 15 ¶14; onani cithunzi pacikuto)
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi Salimo 22 imalimbikitsa bwanji cikhulupililo canga kuti maulosi ena okamba za Mesiya nawonso adzakwanilitsika, monga wopezeka pa Mika 4:4?’
2. Kufufuza Cuma Cauzimu
(Mph. 10)
Sal. 22:22—Kodi masiku ano tingatengele citsanzo ca wamasalimo m’njila ziŵili ziti? (w06 11/1 29 ¶7; w03 9/1 20 ¶1)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutigaŵilako?
3. Kuŵelenga Baibo
(Mph. 4.) Sal. 22:1-19 (th phunzilo 2)
4. Kuyambitsa Makambilano
(Mph. 3) KUNYUMBA NA NYUMBA. (lmd phunzilo 4 mfundo 4)
5. Kubwelelako
(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Pangani ulendo wobwelelako kwa mnzanu amene anavomela kukapezekapo pa Cikumbutso. (lmd phunzilo 4 mfundo 3)
6. Nkhani
(Mph. 5) w20.07 12-13 ¶14-17—Mutu: Mmene Maulosi a m’Baibo Amalimbikitsila Cikhulupililo Cathu. (th phunzilo 20)
Nyimbo 95
7. Zofunikila za Mpingo
(Mph. 15)
8. Phunzilo la Baibo la Mpingo
(Mph. 30) bt mutu. 7 ¶14-18, mabokosi pa mas. 57-58