June 28–July 4
DEUTERONOMO 9-10
Nyimbo 49 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kodi Yehova Mulungu Wanu Akufuna Kuti Muzicita Ciani?”: (10 min.)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
Deut. 9:1-3—Ngakhale kuti ana a Anaki anali “anthu amphamvu ndi aatali,” n’cifukwa ciani Aisiraeli sanafunike kuwaopa? (it-1 103)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Deut. 10:1-22 (th phunzilo 10)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba (Mph. 3) Yambani na makambilano acitsanzo. Gaŵilani cofalitsa ca m’Thuboksi yathu. (th phunzilo 3)
Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Yambani na makambilano acitsanzo. Chulani na kukambilana vidiyo yakuti N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? (koma musaitambitse). (th phunzilo 9)
Phunzilo la Baibo: (Mph. 5) fg phunzilo 12 ¶4-5 (th phunzilo 18)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Maseŵela a pa Vidiyo: Kodi Mukupambanadi?: (Mph. 7) Kukambilana. Onetsani vidiyoyi. Ndiyeno funsani omvetsela mafunso aya: Kodi maseŵela a pa vidiyo angakubweletseleni mavuto otani? Ni zinthu ziti pa umoyo zimene n’zofunika kwambili kuposa maseŵela a pa vidiyo? (Aef. 5:15, 16) Kodi maseŵela a pa vidiyo amene mumasankha amaonetsa bwanji umunthu wanu wam’kati? Kodi mungacite ciani kuti mukhaledi wopambana pa umoyo?
“Muzipanga Zosankha Mwanzelu Pankhani ya Moŵa”: (Mph. 8) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Ganizilani Zotulukapo za Kumwa Moŵa.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb phunzilo 43
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 44 na Pemphelo