May 24-30
NUMERI 34–36
Nyimbo 33 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Thaŵilani kwa Yehova”: (Mph. 10)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
Num. 35:31—N’cifukwa ciani Adamu na Hava sadzapindula na nsembe ya dipo la Yesu? (w91 2/15 13 ¶13)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Num. 34:1-15 (th phunzilo 10)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Mukayamba na makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki, koma mwaluso loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 12)
Ulendo Wobwelelako: (4 min.) Yambani na makambilano acitsanzo. Chulani za vidiyo yakuti N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? (koma musaitambitse). (th phunzilo 9)
Phunzilo la Baibo: (Mph. 5) fg phunzilo 2 ¶9-10 (th phunzilo 19)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Khala Bwenzi la Yehova—Cilango Ni Cikondi: (Mph. 6) Kukambilana. Onetsani vidiyoyi. Ndiyeno, ngati n’kotheka, funsani mafunso ana amene munawasankhilatu. Afunseni kuti: N’cifukwa ciani nthawi zina umafunikila cilango? Kodi cilango cimakupindulitsa bwanji? N’cifukwa ciani Yehova amatipatsa cilango?
“Cilango Cimaonetsa Cikondi ca Yehova”: (Mph. 9) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti “Yehova Amalanga Aliyense Amene Iye Amamukonda”.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb phunzilo 38
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 38 na Pemphelo