Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

May 24-30

NUMERI 34–36

May 24-30

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Thaŵilani kwa Yehova”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • Num. 35:31—N’cifukwa ciani Adamu na Hava sadzapindula na nsembe ya dipo la Yesu? (w91 2/15 13 ¶13)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Num. 34:1-15 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

UMOYO WATHU WACIKHRISTU