May 2-8
1 SAMUELI 27-29
Nyimbo 71 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Mapulani a Davide a Kamenyedwe ka Nkhondo”: (Mph. 10)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
1 Sam. 28:15—Kodi Sauli “anaona” ndani pa cocitikaci? (w10 1/1 20 ¶5-6)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) 1 Sam. 27:1-12 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (Mph. 5) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Ulendo Woyamba: Kuvutika—Yak. 1:13. Nthawi zonse vidiyo ikaima, inunso iimitseni na kufunsa omvetsela mafunso amene aonekela mu vidiyo.
Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 1)
Ulendo Woyamba: (Mph. 5) Yambani na makambilano acitsanzo. Kenako gaŵilani kabuku kakuti Kondwelani na Moyo Kwamuyaya! na kuchulako za vidiyo yakuti N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? (koma musaitambitse) (th phunzilo 6)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Analimbabe pa Cizunzo: (Mph. 15) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi. Ndiyeno, funsani omvetsela mafunso awa: Kodi tiphunzilapo ciyani pa citsanzo ca abale athu pa nthawi ya ulamulilo wa Nazi ku Germany? Tiphunzilapo ciyani pa citsanzo ca abale athu a ku Russia, komanso a m’nthawi ya ulamulilo wakale wa Soviet Union?
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff phunzilo 02
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 94 na Pemphelo