CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Lolani Kuti Yehova Akugwilitseni Nchito
[Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Ezara.]
Yehova analimbikitsa mtima wa Mfumu Koresi kuti amasule Aisiraeli mu ukapolo (Ezara 1:1-3; w22.03 14 ¶1)
Yehova analimbikitsa mitima ya anthu ake kuti akamangenso kacisi (Ezara 1:5; w17.10 26 ¶2)
Ngati ndinu wodzipeleka, Yehova angakupangitseni kukhala ciliconse cimene afuna kuti akwanilitse cifunilo cake.