June 5-11
2 MBIRI 30–31
Nyimbo 87 na Pemphelo
Mawu Oyamba (Mph. 1)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Kusonkhana Pamodzi Kumatipindulila”: (Mph. 10)
Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)
2 Mbiri 30:20—Tiphunzilapo ciyani tikaganizila mmene Yehova anayankhila pemphelo la Hezekiya? (w18.09 6 ¶14-15)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo iti yokupindulilani imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) 2 Mbiri 31:11-21 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Ulendo Woyamba: (Mph. 2) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. (th phunzilo 20)
Ulendo Wobwelelako: (Mph.5) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. M’gaŵileni bulosha yakuti Kondwelani na Moyo Kwamuyaya! na kuyambitsa phunzilo la Baibo m’phunzilo 01. (th phunzilo 18)
Nkhani: (Mph. 5) w19.01 11-12 ¶13-18—Mutu: Tamandani Yehova mwa Kupeleka Ndemanga pa Misonkhano. (th phunzilo 16)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Khala Bwenzi la Yehova—Konzekela Yankho Lako: (Mph. 5) Kukambilana. Onetsani vidiyoyi. Ndiyeno ngati n’zotheka, funsani acicepele m’gulu mafunso awa: Kodi mungakonzekele bwanji kuti mukapelekepo ndemanga pa msonkhano? N’cifukwa ciyani tingakhalebe acimwemwe ngakhale kuti sanatipatseko mwayi wopelekapo ndemanga?
Zimene Gulu Lakwanitsa Kucita: (Mph. 10) Onetsani vidiyo ya Zimene Gulu Lakwanitsa kucita ya June.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff mafunso obweleza a cigawo 3
Mawu Othela (Mph. 3)
Nyimbo 115 na Pemphelo