November 7-13
MIYAMBO 27-31
Nyimbo 86 na Pemphelo
Mau Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU
“Baibo Imakamba za Mkazi Wabwino”: (Mph. 10)
Miy 31:10-12—Amakhala wodalilika (w15 1/15, tsa. 20 ndime 10; w00 2/1-CN, tsa. 31 ndime 2; it-2 tsa. 1183)
Miy. 31:13-27—Amakhala wakhama pa nchito (w00 2/1-CN, tsa. 31 ndime 3-4)
Miy. 31:28-31—Amakhala munthu wauzimu, woyenela kutamandidwa (w15 1/15 tsa. 20 ndime 8; w00 2/1-CN, tsa. 31 ndime 5, 8)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (Mph. 8)
Miy. 27:12—Tingaonetse bwanji kuti ndife ocenjela pamene tisankha zosangulutsa? (w15 7/1 tsa. 8 ndime 3)
Miy 27:21—Kodi “citamando copelekedwa kwa munthu cimasonyeza” bwanji “mmene iye alili”? (w11 8/1-CN, tsa. 29 ndime 2; w06 9/15-CN, tsa. 19 ndime 12)
Kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno kwaniphunzitsa ciani za Yehova?
Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno zimene ningaseŵenzetse mu ulaliki?
Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Miy. 29:11–30:4
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Konzekelani Maulaliki a Mwezi Uno: (Mph. 15) Kukambilana. Tambitsani vidiyo ya citsanzo iliyonse ndi kukambilana zimene mwaphunzilapo. Limbikitsani ofalitsa kukonza ulaliki wawo.
UMOYO WATHU WACIKHIRISTU
“Mwamuna Wake Amadziŵika Pazipata”: (Mph. 5) Nkhani yokambidwa na mkulu.
Zosoŵa za Pampingo: (Mph. 10) Ngati mufuna, kambilanani mfundo zimene mwaphunzila mu Buku Lapacaka. (yb16 masa. 40-41)
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) kr nkhani 3 ndime 13-22, chati pa masa. 36-37, na bokosi pa tsa. 38”
Kubwelelamo na Kuchulako za Mlungu Wotsatila (Mph. 3)
Nyimbo 108 na Pemphelo