MLALIKI 1–6
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU |Muzikondwela Pogwila Nchito Mwakhama
Yehova amafuna kuti tizikondwela na nchito yathu, ndipo amatiuza zimene zingatithandize. Munthu angayambe kukondwela na nchito yake ngati amaiona moyenela.
Kuti muzikondwela na nchito yanu, mufunika . . .
3:13; 4:6
-
kukhala na maganizo oyenela
-
kuganizila mmene nchito yanu imapindulitsila ena
-
kugwila nchito mwakhama. Koma mukakomboka, muzikhala na nthawi yoceza na banja lanu ndi kucita zinthu zauzimu