MLALIKI 7–12
CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU“Kumbukila Mlengi Wako Wamkulu Masiku a Unyamata Wako”
Kumbukilani Mlengi wanu Wamkulu mukali acicepele mwa kuseŵenzetsa maluso anu pom’tumikila
12:1, 13
-
Acicepele ambili ali ndi thanzi ndi mphamvu cakuti angakwanitse kugwila nchito zovuta
-
Acicepele ayenela kuseŵenzetsa nthawi na mphamvu zawo potumikila Yehova pamene akalibe kufooka na ukalamba
Solomo anafotokoza mavuto a ukalamba mwandakatulo
12:2-7
-
Vesi 3: “Akazi oyang’ana pawindo azidzaona mdima”
Kusayang’ana bwino
-
Vesi 4: “Ana onse aakazi azidzaimba nyimbo ndi mau otsika”
Kuvutika kumva
-
Vesi 5: “Zakudya sizidzakoma”
Kusamvela kukoma kwa cakudya