UMOYO NA UTUMIKI WATHU–KABUKU KA MISONKHANO November 2019
Makambilano Acitsanzo
Makambilano otsatizana-tsatizana okamba za colinga ca Mulungu na malonjezo ake a kutsogolo.
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za M’dziko
N’ciani cingatithandize kupewa kutengeka na dziko na zokopa zake kuti tisacoke kwa Yehova?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Pewani Kutengela Maganizo a Dziko Pokonzekela Cikwati
Ni mfundo ziti za m’Baibo zimene zingathandize oloŵa m’banjawo kukonzekela tsiku lapadela limeneli, m’njila yakuti asadzakhale na cikumbumtima covutitsidwa kapena kudziimba mlandu pambuyo pake?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Tifunika Kumenya Nkhondo kuti Tikhalebe m’Coonadi
Kodi tingamenye bwanji “mwamphamvu nkhondo yacikhulupililo”?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Ndikudziŵa Nchito Zako”
Yesu adziŵa zonse zimene zikucitika m’mipingo ndipo amadziŵa ciliconse cokhudza akulu mu mpingo.
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Yehova Adziŵa zimene Tifunikila
N’cifukwa ciani msonkhano wacigawo umakhala cakudya ca panthawi yake? N’ciani cimapangitsa misonkhano ya mkati mwa wiki kukhala yolimbikitsa komanso yothandiza?
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Amuna Anayi Okwela pa Mahosi
Masiku ano tikucitila umboni za amuna anayi ophiphilitsila okwela pa mahosi ochulidwa m’buku la Chivumbulutso. Kodi wokwela pa hosi aliyense akuimila ciani?
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
Yehova Amakonda Munthu Wopeleka Mokondwela
Kodi tingacite bwanji zopeleka kuti ticilikize nchito ya Mboni za Yehova, m’dziko lathu komanso padziko lonse?