November 18-24
CHIVUMBULUTSO 1-3
Nyimbo 15 na Pemphelo
Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Ndikudziŵa Nchito Zako”: (10 min.)
[Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Chivumbulutso.]
Chiv. 1:20—Yesu amadziŵa ciliconse cokhudza akulu mu mpingo (w12 10/15 14 ¶8)
Chiv. 2:1, 2—Yesu adziŵa zimene zikucitika mu mpingo uliwonse (w12 4/15 29 ¶11; w01 1/15 20-21 ¶20)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Chiv. 1:7—Kodi diso lililonse lidzamuona bwanji Yesu pamene “akubwela ndi mitambo”? Nanga zimenezi zidzacitika liti? (kr 226 ¶8, 10)
Chiv. 2:7—Kodi kudya za “mumtengo wa moyo . . .m’paradaiso wa Mulungu” kumatanthauza ciani? (w09 1/15 31 ¶1)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Chiv. 1:1-11 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
Ulendo Wobwelelako Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 2)
Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno, chulani na kukambilana vidiyo yakuti N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? (koma musaitambitse) (th phunzilo 3)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Yehova Adziŵa Zimene Tifunikila”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Lipoti la 2017 la Komiti Yoyang’anila Nchito Yophunzitsa.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 91
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 151 na Pemphelo