November 25–December 1
CHIVUMBULUTSO 4-6
Nyimbo 22 na Pemphelo
Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Amuna Anayi Okwela pa Mahosi”: (10 min.)
Chiv. 6:2—Wokwela pa hosi yoyela ‘anapita kukagonjetsa adani ake’ (wp17.3 4 ¶3, 5)
Chiv. 6:4-6—Ndiyeno panabwela wokwela pa hosi yofiila, ndiponso wokwela pa hosi yakuda (wp17.3 5 ¶2, 4-5)
Chiv. 6:8—Pambuyo pake, panabwela wokwela pa hosi yotuŵa, ndipo Manda anali kumutsatila (wp17.3 5 ¶8-10)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
Chiv. 4:4, 6—Kodi akulu 24 na zamoyo zinayi amaimila ciani? (re 76-77 ¶8; 80 ¶19)
Chiv. 5:5—N’cifukwa ciani Yesu amachulidwa kuti “Mkango wa fuko la Yuda”? (cf 36 ¶5-6)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Chiv. 4:1-11 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Waciŵili: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.
Ulendo Wobwelelako Waciŵili: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 4)
Phunzilo la Baibo: (5 min. olo kucepelapo) lvs 53 ¶15 (th phunzilo 2)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Yehova Amakonda Munthu Wopeleka Mokondwela”: (15 min.) Nkhani yokambiwa na mkulu. Yambani mwa kutambitsa vidiyo yakuti Mmene Mungapelekele Zopeleka pa Intaneti. Fotokozelani ofalitsa kuti angadziŵe zambili zokhudza kucita copeleka mwa kutinika pambali yakuti Zopeleka pa jw.org na pa JW Library kapena kulemba kuti Copeleka.pr418.com pa malo oikapo adresi. Ndiyeno ŵelengani kalata yaciyamikilo yocokela ku Ofesi ya Nthambi yoyamikila zopeleka zimene abale anacita caka catha ca utumiki. Yamikilani mpingo cifukwa ca mtima wawo wocilikiza moolowa manja.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 92
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 43 na Pemphelo