November 4-10
1 YOHANE 1-5
Nyimbo 122 na Pemphelo
Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)
CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
“Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za M’dziko”: (10 min.)
[Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la 1 Yohane.]
1 Yoh. 2:15, 16—‘Ciliconse ca m’dziko . . sicicokela kwa Atate, koma kudziko’ (w05 1/1 10 ¶13)
1 Yoh. 2:17—Dziko likupita limodzi na cilako-lako cake (w13 8/1 27 ¶18)
Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)
1 Yoh. 2:7, 8—Kodi lamulo limene Yohane anakamba pa mavesiwa linakhala bwanji lakale ndiponso latsopano? (w13 9/1 10 ¶14)
1 Yoh. 5:16, 17—Kodi chimo “lobweletsa imfa” n’lotani? (it-1 862 ¶5)
Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?
Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?
Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) 1 Yoh. 1:1–2:6 (th phunzilo 5)
CITANI KHAMA PA ULALIKI
Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Kukamba Mwaumoyo. Ndiyeno, kambilanani phunzilo 11 m’bulosha ya Kuphunzitsa.
Nkhani: (5 min. olo kucepelapo) w04 10/1 29—Mutu: Kodi Yohane anatanthauzanji pa 1 Yohane 4:18, pamene anakamba kuti “cikondi cimene cili cokwanila cimathetsa mantha”? (th phunzilo 7)
UMOYO WATHU WACIKHRISTU
“Pewani Kutengela Maganizo a Dziko Pokonzekela Cikwati”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Maukwati Amene Amalemekeza Yehova.
Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu. 89
Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)
Nyimbo 118 na Pemphelo