CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Zimene Zinathandiza Yobu Kukhalabe Woyela
Yobu anacita pangano na maso ake (Yobu 31:1; w10 4/15 21 ¶8)
Yobu anaganizila zotulukapo za kucita coipa (Yobu 31:2, 3; w08 9/1 11 ¶4)
Iye anali kukumbukila kuti Yehova amaona khalidwe lake (Yobu 31:4; w10 11/15 5-6 ¶15-16)
Kukhala woyela kumatanthauza kukhala waukhondo ndiponso wosaipitsidwa, osati kunja kokha koma na mkati momwe. Timafuna kukhala woyela na mumtima momwe.—Mat. 5:28.