CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU
Munthu Akafa, Kodi Angakhalenso Ndi Moyo?
Palibe munthu angathaŵe imfa kapena kuukitsa akufa (Yobu 14:1, 2, 4, 10; w99 10/15 3 ¶1-3)
Akufa angakhalenso na moyo (Yobu 14:7-9; w15 4/15 32 ¶1-2)
Yehova ali na mphamvu zoukitsa atumiki ake, ndipo amacita kulakalaka kutelo (Yobu 14:14, 15; w11 3/1 22 ¶5)
ZOYENELA KUZISINKHASINKHA: N’cifukwa ciyani Yehova amacita kulakalaka kuti adzaukitse atumiki ake okhulupilika? Kodi izi zimakucititsani kumuona bwanji Yehova?