Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

October 1-7

YOHANE 9-10

October 1-7
  • Nyimbo 25 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Yesu Amasamalila Nkhosa Zake”: (10 min.)

    • Yoh. 10:1-3, 11, 14—Yesu, amene ni “m’busa wabwino,” amazidziŵa nkhosa zake ndipo amasamalila zosoŵa zawo mokwanila (“Khola la Nkhosanwtsty zithunzi; w11 5/15 mape. 7-8 pala. 5)

    • Yoh. 10:4, 5—Nkhosa zimadziŵa mawu a Yesu, osati a alendo (cf mape. 124-125 pala. 17)

    • Yoh. 10:16—Nkhosa za Yesu zimakhala mogwilizana (“kuzitenganwtsty mfundo younikila)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yoh 9:38—N’cifukwa ciani wopempha-pempha wakhungu anagwadila Yesu? (“anam’gwadila iyenwtsty mfundo younikila)

    • Yoh. 10:22—N’cifukwa ciani Ayuda anali kucita Cikondwelelo ca Kupeleka Kacisi kwa Mulungu? (“Cikondwelelo ca Kupeleka Kacisinwtsty mfundo younikila)

    • Kodi kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Yoh. 9:1-17

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Kubwelelako Koyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) fg phunzilo 14 mapa. 1-2

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 62

  • Zofunikila za Mpingo: (15 min.)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy Mutu 37

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 3 na Pemphelo