Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

September 5-11

SALIMO 119

September 5-11
  • Nyimbo 48 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • Muzitsatila Cilamulo ca Yehova”: (Mph. 10)

    • Sal. 119:1-8—Kutsatila cilamulo ca Mulungu n’kumene kumatipatsa cimwemwe ceni-ceni (w05 4/15-CN, tsa. 10 ndime 3-4)

    • Sal. 119:33-40—Mawu a Mulungu amatithandiza kuti tikhale olimba mtima polimbana ndi ziyeso (w05 4/15-CN, tsa. 12 ndime 12)

    • Sal. 119:41-48—Kudziŵa molondola Mawu a Mulungu kumatithandiza kulalikila molimba mtima (w05 4/15-CN, tsa. 13 ndime 13-14)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (Mph. 8)

    • Sal. 119:71—Kodi kuzunzidwa kungakhale kokoma m’njila yanji? (w06 9/1-CN, tsa. 14 ndime 4)

    • Sal. 119:96—Kodi mawu akuti, “Ndaona kuti zinthu zonse zabwino kwambili zili ndi malile” atanthauza ciani? (w06 9/1-CN, tsa. 14 ndime 5)

    • Kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno kwaniphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ningaseŵenzetse mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibulo: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Sal. 119:73-93

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Konzekelani Maulaliki a Mwezi Uno: (Mph. 15) Kukambilana. Tambitsani mavidiyo a maulaliki acitsanzo, ndipo kambilanani mfundo zake. Limbikitsani ofalitsa kukonza ulaliki wawo.

UMOYO WATHU WACIKHIRISTU

  • Nyimbo 69

  • Mukapeza Mwana Panyumba”: (Mph. 5) Nkhani.

  • Zosoŵa za Pampingo: (Mph. 10) Ngati mufuna, mungakambilane zimene munaphunzila mu Buku Lapacaka. (yb16 masa. 59-62)

  • Phunzilo la Baibulo la Mpingo: (Mph. 30) ia nkhani 23 ndime 15-29, ndi kubwelelamo tsa. 204

  • Kubwelelamo ndi Kuchulako za Mlungu Wotsatila (Mph. 3)

  • Nyimbo 13 na Pemphelo