Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MASALIMO 142-150

“Yehova Ndi Wamkulu ndi Woyenela Kutamandidwa Kwambili”

“Yehova Ndi Wamkulu ndi Woyenela Kutamandidwa Kwambili”

145:1-5

Pamene anaona kuti ukulu wa Yehova ni wosasanthulika, Davide analimbikitsidwa kumutamanda kwamuyaya

145:10-12

Mofanana ndi Davide, atumiki okhulupilika a Yehova amakamba za nchito zake zamphamvu tsiku lililonse

145:14

Davide sanakaikile kuti Yehova amafuna kusamalila atumiki ake onse ndi kuti ali ndi mphamvu zocita zimenezo