Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Maulaliki a Citsanzo

Maulaliki a Citsanzo

NSANJA YA MLONDA

Funso: Aliyense amafuna citonthozo nthawi zina. Kodi n’kuti kumene tingacipeze?

Lemba: 2 Akor. 1:3, 4

Cogaŵila: Magazini iyi ya Nsanja ya Mlonda ifotokoza mmene Mulungu amatitonthozela.

NSANJA YA MLONDA (cikuto cothela)

Funso: Anthu ena amaganiza kuti Ufumu wa Mulungu ni mtima wa munthu. Ena amaganiza kuti ndi mtendele umene anthu adzabweletsa padziko lonse. Inu muganiza bwanji?

Lemba: Dan. 2:44

Cogaŵila: Baibulo imakamba kuti Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni. Nkhani iyi ifotokoza zinthu zina zambili zimene Baibulo imakamba ponena za Ufumu wa Mulungu.

PHUNZITSANI COONADI

Funso: Tidziŵa bwanji kuti Mulungu amatidela nkhawa?

Lemba: 1 Pet. 5:7

Mfundo ya Coonadi: Mulungu amafuna kuti tizipemphela kwa iye cifukwa amatidela nkhawa.

KONZANI ULALIKI WANU

Funso:

Lemba:

Cogaŵila: