October 14-20
MASALIMO 96-99
Nyimbo 66 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)
1. “Muzilengeza Uthenga Wabwino”!
(Mph. 10)
Muzilalikila uthenga wabwino (Sal. 96:2; w11-CN 3/1 6 ¶1-2)
Uzani anthu uthenga wabwino wa Tsiku la Ciweluzo (Sal. 96:12, 13; w12 9/1 16 ¶1)
Auzeni colinga ca Yehova codzaza dziko lapansi na anthu amene amatamanda dzina lake (Sal. 99:1-3; w12-CN 9/15 12 ¶18-19)
2. Kufufuza Cuma Cauzimu
(Mph. 10)
Sal. 96:1—Kodi nthawi zambili mawu akuti “nyimbo yatsopano” akagwilitsidwa nchito amaonetsa ciyani? (it-2-E 994)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?
3. Kuŵelenga Baibo
(Mph. 4) Sal. 98:1–99:9 (th phunzilo 11)
4. Kudzipeleka—Mmene Yesu Anacitila Zimenezi
(Mph. 7) Kukambilana. Tambitsani VIDIYO, kenako kambilanani lmd phunzilo 10 mfundo 1-2.
5. Kudzipeleka—Tengelani Citsanzo ca Yesu
(Mph. 8) Makambilano ozikika mu lmd phunzilo 10 mfundo 3-5, komanso mbali yakuti “Onaninso Malemba Awa.”
Nyimbo 9
6. Zofunikila za Mpingo
(Mph. 15)
7. Phunzilo la Baibo la Mpingo
(Mph. 30) bt mutu 16 ¶10-18