September 9-15
MASALIMO 82-84
Nyimbo 80 na Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)
1. Muziyamikila Mwayi wa Utumiki Umene Muli Nawo
(Mph. 10)
Timaukonda kwambili utumiki wathu (Sal. 84:1-3; wp16.6 8 ¶2-3)
Muzisangalala na utumiki umene muli nawo m’malo mongolakalaka umene mulibe (Sal. 84:10; w08-CN 7/15 30 ¶3-4)
Yehova ni wabwino kwa onse amene amam’tumikila mokhulupilika (Sal. 84:11; w20.01 17 ¶12)
Utumiki uliwonse uli na madalitso na zovuta zake. Mukamaganizila kwambili pa madalitso, mudzapeza cimwemwe pocita utumiki uliwonse.
2. Kufufuza Cuma Cauzimu
(Mph. 10)
Sal. 82:3—N’cifukwa ciyani kuonetsa cikondi kwa “ana amasiye” mu mpingo n’kofunika? (it-1-E 816)
Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?
3. Kuŵelenga Baibo
(Mph. 4) Sal. 82:1–83:18 (th phunzilo 2)
4. Cifundo—Mmene Yesu Anaonetsela Khalidwe Limeneli
(Mph. 7) Kukambilana. Tambitsani VIDIYO, kenako kambilanani lmd phunzilo 9 mfundo 1-2.
5. Cifundo—Tengelani Citsanzo ca Yesu
(Mph. 8) Kukambilana. Seŵenzetsani lmd phunzilo 9 mfundo 3-5 komanso mbali yakuti “Onaninso Malemba Awa.”
Nyimbo 57
6. Zofunikila za Mpingo
(Mph. 15)
7. Phunzilo la Baibo la Mpingo
(Mph. 30) bt mutu 15 ¶8-12, bokosi pa tsa. 118