Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Ziŵelengelo Zonse za mu 2019

Ziŵelengelo Zonse za mu 2019
  • Nthambi za Mboni za Yehova: 87

  • Ciŵelengelo ca Maiko ocitila Lipoti: 240

  • Ciŵelengelo ca Mipingo yonse: 119,712

  • Opezeka pa Cikumbutso Padziko Lonse: 20,919,041

  • Amene Anadya Ziphiphilitso Padziko Lonse: 20,526

  • Ofalitsa Onse Amene Anagwila Nchito Yolalikila *: 8,683,117

  • Avaleji ya Ofalitsa Amene Anali kulalikila Mwezi Uliwonse: 8,471,008

  • Kuwonjezeka kwa Ofalitsa Kucokela mu 2018: 1.3%

  • Onse Amene Anabatizika *: 303,866

  • Avaleji ya Apainiya * Mwezi Uliwonse: 1,277,738

  • Avaleji ya Apainiya Othandiza Mwezi Uliwonse: 464,980

  • Maola Onse Amene Tinathela Mu Utumiki: 2,088,560,437

  • Avaleji ya Maphunzilo a Baibo * Mwezi Uliwonse: 9,618,182

M’caka ca utumiki ca 2019, * Mboni za Yehova zinagwilitsa nchito ndalama zoposa madola 224 miliyoni posamalila apainiya apadela, amishonale komanso oyang’anila madela pa utumiki wawo. ▪ Padziko lonse pali abale na alongo okwana 20,858, amene akutumikila m’maofesi a nthambi. Onse amenewa ali m’Gulu Lapadziko Lonse la Atumiki Apadela a Nthawi Zonse a Mboni za Yehova.

^ ndime 7 Wofalitsa ni munthu amene amalalikila mwakhama uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu. (Mateyu 24:14) Kuti mudziŵe mmene timapezela ciŵelengelo cimeneci, onani nkhani yakuti “Kodi a Mboni za Yehova Alipo Angati Padziko Lonse?” pa jw.org ku chichewa

^ ndime 10 Kuti mudziŵe zimene mungacite kuti mubatizidwe n’kukhala wa Mboni za Yehova, onani nkhani yakuti “Kodi Ndingatani Kuti Ndikhale wa Mboni za Yehova?” pa jw.org ku chichewa.

^ ndime 11 Mpainiya ni wa Mboni wacitsanzo cabwino amene amadzipeleka kuti azilalikila uthenga wabwino kwa maola ena ake mwezi uliwonse.

^ ndime 14 Kuti mudziŵe zambili, onani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi Phunzilo la Baibulo N’ciani?

^ ndime 15 Caka ca utumiki ca 2019 cinayamba pa September 1, 2018, ndipo cinasila pa August 31, 2019.