Onetsani Cikhulupililo!
YOHANE 14:1
M’MAŴA
-
8:30 Nyimbo Zamalimba
-
8:40 Nyimbo Na. 118 na Pemphelo
-
8:50 Onetsani Cikhulupililo!—Motani, Cifukwa Ciani?
-
9:05 Yosiyilana: Tengelani Citsanzo ca Amene Anaonetsa Cikhulupililo
-
• Isaki na Rabeka
-
• Esitere
-
• Timoteyo
-
-
10:05 Nyimbo Na. 60 na Zilengezo
-
10:15 “Tili ndi Cikhulupililo, Cotelo Tikulankhula”
-
10:30 Kudzipatulila na Ubatizo
-
11:00 Nyimbo Na. 52
MASANA
-
12:10 Nyimbo Zamalimba
-
12:20 Nyimbo Na. 9 na Pemphelo
-
12:30 Nkhani ya Anthu Onse: Onetsani Cikhulupililo mwa Mulungu “Amene Sanganame”
-
13:00 Cidule ca Nsanja ya Mlonda
-
13:30 Nyimbo Na. 54 na Zilengezo
-
13:40 Yosiyilana: ‘Yendani mwa Cikhulupililo’ Tsiku Lililonse
-
• “Musamade Nkhawa”
-
• “Muzigwilitsa Nchito Bwino Nthawi Yanu”
-
• Pitilizani Kusakhala “Mbali ya Dziko”
-
-
14:40 “Yehova Amadziŵa Anthu Ake”
-
15:15 Nyimbo Na. 7 na Pemphelo