Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Tsiku Loyamba

Tsiku Loyamba

“Tiwonjezeleni cikhulupililo”​—Luka 17:5

M’MAŴA

  • 9:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 5 na Pemphelo

  • 9:40 NKHANI YA CHEYAMANI: Kodi Cikhulupililo N’camphamvu Motani? (Mateyu 17:19, 20; Aheberi 11:1)

  • 10:10 YOSIYILANA: Cifukwa Cake Timakhulupilila . . .

    • • Kuti Mulungu Aliko (Aefeso 2:1, 12; Aheberi 11:3)

    • • Mawu a Mulungu (Yesaya 46:10)

    • • Miyezo ya Mulungu ya Makhalidwe Abwino (Yesaya 48:17)

    • • Cikondi ca Mulungu (Yohane 6:44)

  • 11:05 Nyimbo Na. 37 na Zilengezo

  • 11:15 KUŴELENGA BAIBO MONGA SEŴELO: Nowa​—Cikhulupililo Cinamusonkhezela Kumvela Mulungu (Genesis 6:1–8:22; 9:8-16)

  • 11:45 ‘Khalani ndi Cikhulupililo, Osakayika’ (Mateyu 21:21, 22)

  • 12:15 Nyimbo Na. 118 na Kupumula

MASANA

  • 13:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 13:45 Nyimbo Na. 2

  • 13:50 YOSIYILANA: Yang’anani Cilengedwe Kuti Mulimbitse Cikhulupililo Canu

    • • Nyenyezi (Yesaya 40:26)

    • • Nyanja Zamcele (Salimo 93:4)

    • • Nkhalango (Salimo 37:10, 11, 29)

    • • Mphepo na Madzi (Salimo 147:17, 18)

    • • Zolengedwa za m’Nyanja (Salimo 104:27, 28)

    • • Matupi Athu (Yesaya 33:24)

  • 14:50 Nyimbo Na. 148 na Zilengezo

  • 15:00 Nchito Zamphamvu za Yehova Zimalimbitsa Cikhulupililo (Yesaya 43:10; Aheberi 11:32-35)

  • 15:20 YOSIYILANA: Tengelani Citsanzo ca Anthu a Cikhulupililo, Osati Opanda Cikhulupililo

    • • Abele, Osati Kaini (Aheberi 11:4)

    • • Inoki, Osati Lameki (Aheberi 11:5)

    • • Nowa, Osati Anthu a m’Nthawi Yake (Aheberi 11:7)

    • • Mose, Osati Farao (Aheberi 11:24-26)

    • • Ophunzila a Yesu, Osati Afarisi (Machitidwe 5:29)

  • 16:15 “Pitilizani Kudziyesa Kuti Muone Ngati Mukadali Olimba m’Cikhulupililo”​—Motani? (2 Akorinto 13:5, 11)

  • 16:50 Nyimbo Na. 119 na Pemphelo