Pezani Mayankha pa Mafunso Awa
1. Kodi tingaonetse bwanji kuti timayamikiladi malo athu m’banja la Yehova? (Aef. 4:3)
2. Kodi tingapangitse bwanji ena kumva kuti ni olandilidwa? Nanga n’cifukwa ciyani tiyenela kucita zimenezo? (Aroma 15:7)
3. Kodi tingathandize bwanji anthu ambili mmene tingathele kuti abwele m’banja la Yehova? (Aef. 2:17; 6:15)
4. Kodi tingalimbikitse bwanji mtendele? (Aef. 4:29; 5:1, 2; 6:13)
5. Kodi tingakulitse bwanji cikondi pa banja lathu lauzimu? (Aef. 1:15, 16)
© 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
CA-copgm23-CIN