Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Tsiku Loyamba

Tsiku Loyamba

“Yehova adzadalitsa anthu ake ndi mtendele.”—Salimo 29:11

M’maŵa

  • 8:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 86 na Pemphelo

  • 8:40 NKHANI YA CHEYAMANI: Yehova ni “Mulungu Amene Amapatsa Mtendele” (Aroma 15:33; Afilipi 4:6, 7)

  • 9:10 YOSIYILANA: Mmene Cikondi Cimabweletsela Mtendele Weniweni

    • • Kukonda Mulungu (Mateyu 22:37, 38; Aroma 12:17-19)

    • • Kukonda Anansi Athu (Mateyu 22:39; Aroma 13:8-10)

    • • Kukonda Mawu a Mulungu (Salimo 119:165, 167, 168)

  • 10:05 Nyimbo Na. 24 na Zilengezo

  • 10:15 KUŴELENGA BAIBO MONGA SEŴELO: Yakobo—Munthu Wokonda Mtendele (Genesis 26:12–33:11)

  • 10:45 “Nchito ya Cilungamo Ceniceni Idzakhala Mtendele” (Yesaya 32:17; 60:21, 22)

  • 11:15 Nyimbo Na. 97 na Kupumula

Masana

  • 12:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 144

  • 12:50 YOSIYILANA: Kondwelani na Malonjezo a Mulungu Okamba za Mtendele

    • • “Atumiki Anga Adzadya . . . Atumiki Anga Adzamwa” (Yesaya 65:13, 14)

    • • “Iwo Adzamanga Nyumba n’Kukhalamo,” Ndipo “Adzabzala Minda ya Mpesa.” (Yesaya 65:21-23)

    • • “Mmbulu ndi Mwana wa Nkhosa Zidzadyela Pamodzi” (Yesaya 11:6-9; 65:25)

    • • “Palibe Munthu Wokhala m’Dzikolo Amene Adzanene Kuti: ‘Ndikudwala’” (Yesaya 33:24; 35:5, 6)

    • • “Iye Adzameza Imfa Kwamuyaya” (Yesaya 25:7, 8)

  • 13:50 Nyimbo Na. 35 na Zilengezo

  • 14:00 YOSIYILANA: Zofunikila Kuti M’banja Mukhale Mtendele

    • • Kuonetsana Cikondi na Ulemu (Aroma 12:10)

    • • Kukambilana Momasuka (Aefeso 5:15, 16)

    • • Kucita Zinthu Monga Timu (Mateyu 19:6)

    • • Kulambila Yehova Capamodzi (Yoswa 24:15)

  • 14:55 Thandizilani “Kalonga Wamtendele” Mokhulupilika (Yesaya 9:6, 7; Tito 3:1, 2)

  • 15:15 Musasoceletsedwe na Mtendele Wabodza! (Mateyu 4:1-11; Yohane 14:27; 1 Atesalonika 5:2, 3)

  • 15:50 Nyimbo Na. 112 na Pemphelo Lothela