Loŵani mu Mpumulo wa Mulungu!
AHEBERI 4:11
M’maŵa
-
08:40 Nyimbo Zamalimba
-
08:50 Nyimbo Na. 87 na Pemphelo
-
09:00 Loŵani mu Mpumulo wa Mulungu —Motani?
-
09:15 Kodi “Mawu a Mulungu ndi Amoyo”—M’njila Yotani?
-
09:30 Pitilizani Kudalila Yehova Kuti Akutsogoleleni
-
09:55 Nyimbo Na. 89 na Zilengezo
-
10:05 Yehova Amadalitsa anthu Omvela
-
10:35 Kudzipatulila na Ubatizo
-
11:05 Nyimbo Na. 32
Masana
-
12:20 Nyimbo Zamalimba
-
12:30 Nyimbo Na. 49
-
12:35 Zocitika
-
12:45 Cidule ca Nsanja ya Mlonda
-
13:15 Nkhani Yosiyilana: Amakondweletsa Mtima wa Yehova!
-
• Acinyamata
-
• Alongo
-
• Okalamba
-
-
14:00 Nyimbo Na. 38 na Zilengezo
-
14:10 Pezani Cimwemwe mu Utumiki Wanu kwa Yehova
-
14:55 Nyimbo Na. 118 na Pemphelo