Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

3-B

Chati: Aneneli ndi Mafumu a Yuda ndi a Isiraeli (Mbali 2)

Chati: Aneneli ndi Mafumu a Yuda ndi a Isiraeli (Mbali 2)

Mafumu a Ufumu wa Kumwela (Kupitililza)

777 B.C.E.

Yotamu: zaka 16

762

Ahazi: zaka 16

746

Hezekiya: zaka 29

716

Manase: zaka 55

661

Amoni: zaka ziŵili

659

Yosiya: zaka 31

628

Yehoahazi: miyezi itatu

Yehoyakimu: zaka 11

618

Yehoyakini: miyezi itatu ndi masiku 10

617

Zedekiya: miyezi 11

607

Ababulo motsogozedwa ndi Nebukadinezara aononga Yerusalemu ndi kacisi wake. Zedekiya mfumu yomaliza pa mafumu apadziko lapansi a m’banja la Davide acotsedwa pa ufumu

Mafumu a Ufumu wa Kumpoto (Kupitililza)

c. 803 B.C.E.

Zekariya: analamulila miyezi 6 yokha

N’zotheka kuti panthawiyi Zekariya anayamba kulamulila, komabe ufumu wake unazatsimikizilidwe ca m’ma c. 792

c. 791

Salumu: Mwezi umodzi

c. 780

Manehemu: zaka 10

Pekahiya: zaka ziŵili

c. 778

Peka: zaka 20

c. 758

Hoshiya: zaka 9 kucokela mu c. 748

c. 748

Zioneka kuti ulamulilo wa Hoshiya unakhazikika ndipo n’zothekanso kuti anali kulandila thandizo kucokela kwa mfumu ya Asuri Tigilati Pilesere III m’ma c. 748

740

Asuri agonjetsa Samaliya, ayamba kulamulila Aisiraeli; ufumu wa kumpoto wa mafuko 10 a Isiraeli ukutha

  • Mundanda wa Aneneli

  • Yesaya

  • Mika

  • Zefaniya

  • Yeremiya

  • Nahamu

  • Habakuku

  • Danieli

  • Ezekieli

  • Obadiya

  • Hoseya