12
Kacisi Amene Solomo Anamanga
-
Maonekedwe a Kacisi
-
1 Malo Oyela Koposa (1 Maf. 6:16, 20)
-
2 Malo Oyela (2 Mbiri 5:9)
-
3 Zipinda Zakudenga (1 Mbiri 28:11)
-
4 Zipinda za Mbali (1 Maf. 6:5, 6, 10)
-
5 Yakini (1 Maf. 7:21; 2 Mbiri 3:17)
-
6 Boazi (1 Maf. 7:21; 2 Mbiri 3:17)
-
7 Khonde (1 Maf. 6:3; 2 Mbiri 3:4) (Utali wake wosatsimikizika)
-
8 Guwa la Nsembe la Mkuwa (2 Mbiri 4:1)
-
9 Nsanja Yamkuwa (2 Mbiri 6:13)
-
10 Bwalo Lamkati (1 Maf. 6:36)
-
11 Tanki Yamkuwa (1 Maf. 7:23)
-
12 Zotengela (1 Maf. 7:27)
-
13 Khomo la Mbali (1 Maf. 6:8)
-
14 Zipinda Zodyela (1 Mbiri 28:12)