16-B
Mlungu Womaliza wa Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Mbali 2)
Nisani 12
KULOŴA KWA DZUŴA (Masiku Aciyuda anali kuyamba ndi kutha poloŵa dzuŵa)
KUTULUKA KWA DZUŴA
-
Tsiku laphee ndi ophunzila ake
-
Yudasi akonza ciwembu com’peleka
-
Luka 22:1-6
KULOŴA KWA DZUŴA
Nisani 13
KULOŴA KWA DZUŴA
KUTULUKA KWA DZUŴA
-
Petulo ndi Yohane akonzekela Pasika
-
Yesu ndi atumwi ena afika madzulo
-
Luka 22:7-13
KULOŴA KWA DZUŴA
Nisani 14
KULOŴA KWA DZUŴA
-
Akudya Pasika ndi atumwi
-
Asambitsa mapazi a atumwi
-
Auza Yudasi kuti acoke
-
Ayambitsa mwambo wa Cakudya Camadzulo ca Ambuye
-
Luka 22:14-38
-
Yohane 13:1–17:26
-
Apelekedwa ndi kumangidwa m’munda wa Getsemani
-
Atumwi athaŵa
-
Azengedwa mlandu ndi Khoti Lalikulu kunyumba kwa Kayafa
-
Petulo akana Yesu
-
Luka 22:39-65
-
Yohane 18:1-27
KUTULUKA KWA DZUŴA
-
Aonekelanso pamaso pa Khoti Lalikulu la Ayuda
-
Apita naye kwa Pilato, ndiyeno kwa Herode, am’bwezanso kwa Pilato
-
Aweluzidwa ndipo aphedwe kumalo ochedwa Gologota
-
Akufa masana ca m’ma 3 koloko
-
Acotsa mtembo ndi kuuika m’manda
-
Luka 22:66–23:56
-
Yohane 18:28-40; 19:1-42
KULOŴA KWA DZUŴA
Nisani 15 (Sabata)
KULOŴA KWA DZUŴA
KUTULUKA KWA DZUŴA
-
Pilato alamula kuti aike asilikali pa manda a Yesu
KULOŴA KWA DZUŴA
Nisani 16
KULOŴA KWA DZUŴA
-
Agulilapo zonukhilitsa manda zina
KUTULUKA KWA DZUŴA
-
Aukitsidwa
-
Aonekela kwa ophunzila ake
-
Luka 24:1-49
-
Yohane 20:1-25
KULOŴA KWA DZUŴA