4-D
Zocitika Zazikulu Paumoyo wa Yesu wa Padziko—Utumiki Waukulu wa Yesu m’Galileya (Mbali 2)
NTHAWI |
MALO |
COCITIKA |
MATEYU |
MALIKO |
LUKA |
YOHANE |
---|---|---|---|---|---|---|
31 kapena 32 |
Kaperenao |
Yesu apeleka mafanizo a Ufumu |
8:4-18 |
|||
Nyanja ya Galileya |
Atontholetsa cimphepo camphamvu ali m’ngalawa |
8:22-25 |
||||
Dela la Gadara |
Athamangitsila ziŵanda m’nkhumba |
8:26-39 |
||||
Mwina ku Kaperenao |
Acilitsa mai wodwala nthenda yotaya magazi; aukitsa mwana wa Yairo |
8:40-56 |
||||
Kaperenao (?) |
Acilitsa wakhungu ndi wosalankhula |
|||||
Nazareti |
Am’kananso ku dela la kwao |
|||||
Galileya |
Ulendo wacitatu wa ku Galileya; afutukula nchito mwa kutuma atumwi |
9:1-6 |
||||
Tiberiyo |
Herode adula mutu Yohane; Herode athedwa nzelu ndi Yesu |
9:7-9 |
||||
32, pafupi ndi Pasika (Yoh 6:4) |
Kaperenao (?); NE pafupi ndi Nyanja ya Galileya |
Atumwi abwele kucoka paulendo wolalikila; Yesu adyetsa amuna 5,000 |
9:10-17 |
6:1-13 |
||
NE pafupi ndi Nyanja ya Galileya; Genesarete |
Anthu ayesa kulonga Yesu Ufumu; ayenda panyanja; acilitsa ambili |
6:14-21 |
||||
Kaperenao |
Akuti ndiye “cakudya copatsa moyo”; ambili akhumudwa ndi kumusiya |
6:22-71 |
||||
32, pambuyo pa Pasika |
Mwina ku Kaperenao |
Avumbula miyambo ya anthu |
7:1 |
|||
Foinike; Dekapole |
Acilitsa mwana wamkazi wacisurofoinike; adyetsa amuna 4,000 |
|||||
Magadani |
Sanapeleke cizindikilo ciliconse kupatulapo ca Yona |