4-C
Zocitika Zazikulu Paumoyo wa Yesu wa Padziko—Utumiki Waukulu wa Yesu m’Galileya (Mbali 1)
NTHAWI |
MALO |
COCITIKA |
MATEYU |
MALIKO |
LUKA |
YOHANE |
---|---|---|---|---|---|---|
30 |
Galileya |
Coyamba Yesu alengeza kuti “Ufumu wakumwamba wayandikila” |
4:14, 15 |
4:44, 45 |
||
Kana; Nazareti; Kaperenao |
Acilitsa mwana wa mkulu wa boma; aŵelenga mpukutu wa Yesaya; akanidwa; apita ku Kaperenao |
4:16-31 |
4:46-54 |
|||
Nyanja ya Galileya, pafupi ndi Kaperenao |
Aitana ophunzila anai: Simoni ndi Andireya, Yakobo ndi Yohane |
5:1-11 |
||||
Kaperenao |
Acilitsa apongozi a Simoni ndi ena |
4:31-41 |
||||
Galileya |
Ulendo woyamba wa ku Galileya ndi ophunzila ake anai |
4:42, 43 |
||||
Acilitsa wakhate; khamu la anthu limutsatila |
5:12-16 |
|||||
Kaperenao |
Acilitsa wopuwala |
5:17-26 |
||||
Aitana Mateyu; akudya ndi osonkhetsa msonkho; funso la kusala kudya |
5:27-39 |
|||||
Yudeya |
Alalikila m’sunagoge |
|||||
31, Pasika |
Yerusalemu |
Acilitsa mwamuna wodwala ku Betesida; Ayuda afuna kumupha |
5:1-47 |
|||
Abwelako ku Yerusalemu (?) |
Ophunzila ake abudula ngala za tiligu pa Sabata; Yesu “Mbuye wa Sabata” |
6:1-5 |
||||
Galileya; Nyanja ya Galileya |
Acilitsa wopuwala dzanja pa Sabata; khamu limutsatila; Acilitsa ambili |
6:6-11 |
||||
Phili pafupi ndi Kaperenao |
Asankha atumwi 12 |
6:12-16 |
||||
Pafupi ndi Kaperenao |
Ulaliki wa paphili |
6:17-49 |
||||
Kaperenao |
Acilitsa wanchito wa kapitawo wa asilikali |
7:1-10 |
||||
Naini |
Aukitsa mwana wa mkazi wamasiye |
7:11-17 |
||||
Tiberiyo; Galileya (Naini kapena capafupi) |
Yohane aikidwa m’ndende atumiza ophunzila ake kwa Yesu; ayamikila Yohane |
7:18-35 |
||||
Galileya (Naini kapena capafupi) |
Mai wocimwa athila mafuta kumapazi ake; fanizo la nkhongole |
7:36-50 |
Galileya Ulendo waciŵili wokalalikila, ndi ophunzila 12 |
8:1-3 |
||
Atulutsa ziŵanda; cimo losakhululukidwa |
||||||
Sanapeleke cizindikilo koma ca Yona |
||||||
Amai ake ndi abale ake afika; anena kuti ophunzila ake ndiwo abale ake |
8:19-21 |