Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

4-F

Zocitika Zazikulu Paumoyo wa Yesu wa Padziko—Utumiki wa Yesu Wakumapeto Kum’maŵa kwa Yorodano

Zocitika Zazikulu Paumoyo wa Yesu wa Padziko—Utumiki wa Yesu Wakumapeto Kum’maŵa kwa Yorodano

NTHAWI

MALO

COCITIKA

MATEYU

MALIKO

LUKA

YOHANE

32, Pambuyo pa Cikondwelelo Copeleka Kacisi

Betaniya kutsidya la Yorodano

Apita kumene Yohane anali kubatiza; ambili akhulupilila Yesu

     

10:40-42

Pereya

Aphunzitsa mizinda ndi m’midzi, ulendo wa kufupi ndi Yerusalemu

   

13:22

 

Awalimbikitsa kuloŵa pa khomo lopapatiza; amvela cisoni Yerusalemu

   

13:23-35

 

Mwina ku Pereya

Aphunzitsa kudzicepetsa; mafanizo: malo olemekezeka kwambili ndi alendo amene anapeleka zifukwa zokanila

   

14:1-24

 

Kuwelengela mtengo wokhala wophunzila

   

14:25-35

 

Mafanizo: nkhosa yotaika, ndalama yotaika, mwana woloŵelela

   

15:1-32

 

Mafanizo: mtumiki wosakhulupilika, munthu wacuma ndi Lazaro

   

16:1-31

 

Aphunzitsa za kukhumudwitsa, kukhululukila, ndi cikhulupililo

   

17:1-10

 

Betaniya

Imfa ya Lazaro ndi kuukitsidwa kwake

     

11:1-46

Yerusalemu; Efuraimu

Akonza ciwembu copha Yesu; acoka

     

11:47-54

Samariya; Galileya

Acilitsa akhate 10; awauza mmene Ufumu wa Mulungu udzabwelela

   

17:11-37

 

Samariya kapena Galileya

Mafanizo: mkazi wamasiye wolimbikila, Mfalisi ndi wokhometsa msonkho

   

18:1-14

 

Pereya

Aphunzitsa za cikwati ndi kulekana

19:1-12

10:1-12

   

Adalitsa ana

19:13-15

10:13-16

18:15-17

 

Funso la munthu wa cuma; fanizo la anganyu m’munda wa mpesa ndi malipilo ofanana

19:16–20:16

10:17-31

18:18-30

 

Mwina ku Pereya

Kacitatu anenelatu za imfa yake

20:17-19

10:32-34

18:31-34

 

Pempho lakuti Yakobo ndi Yohane akakhale ndi udindo mu Ufumu

20:20-28

10:35-45

   

Yeriko

Yeriko Pamene anali kupitamo, anacilitsa amuna aŵili akhungu; acezela Zakeyo; fanizo la ndalama

20:29-34

10:46-52

18:35–19:28